Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 107:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Chifukwa anachita zinthu mopandukira+ mawu a Mulungu,+

      Ndipo ananyoza malangizo a Wam’mwambamwamba.+

  • Yesaya 1:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Tsoka kwa mtundu wochimwa,+ anthu olemedwa ndi zolakwa, mbewu yochita zoipa,+ ana obweretsa chiwonongeko.+ Iwo amusiya Yehova.+ Achitira Woyera wa Isiraeli zinthu zopanda ulemu,+ ndipo abwerera m’mbuyo.+

  • Yesaya 30:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Pakuti amenewa ndi anthu opanduka,+ ana ochita zachinyengo,+ amene safuna kumva malamulo a Yehova,+

  • Yeremiya 16:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ndipo inu mwachita zinthu zoipa kwambiri kuposa makolo anu.+ Aliyense wa inu akupitiriza kuumitsa mtima+ wake woipawo ndipo simukundimvera.+

  • Maliro 1:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Taonani, inu Yehova. Inetu zandivuta. M’mimba mwanga mukubwadamuka.+

      Mtima wanga wasweka,+ pakuti ndapanduka kwambiri.+

      Panja, lupanga lapha+ ana. M’nyumba, anthu akufanso.+

  • Danieli 9:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Inu Yehova Mulungu wathu, ndinu wachifundo+ ndi wokhululuka,+ koma ife takupandukirani.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena