Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 19:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 N’zolakalakika kuposa golide, kuposa golide wambiri woyengeka bwino.+

      N’zotsekemera* kuposa uchi,+ inde kuposa uchi umene ukukha m’zisa.+

  • Salimo 119:103
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 103 Mawu anu amatsekemera m’kamwa mwanga,

      Kuposa mmene uchi umakomera!+

  • Yeremiya 15:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Mawu anu anandipeza ndipo ndinawadya.+ Mawu anu amandikondweretsa+ ndi kusangalatsa mtima wanga,+ pakuti ine ndimatchedwa ndi dzina lanu,+ inu Yehova Mulungu wa makamu.+

  • Chivumbulutso 10:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Choncho, ndinapita kwa mngeloyo n’kumuuza kuti andipatse mpukutu waung’onowo. Iye anandiuza kuti: “Tenga mpukutuwu udye.+ Ukupweteketsa m’mimba, koma m’kamwa mwako ukhala wozuna ngati uchi.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena