Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 12:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Iye anawauza kuti: “Mvetserani mawu anga. Pakanakhala mneneri wa Yehova pakati panu, ndikanamudziwitsa za ine m’masomphenya,+ ndipo ndikanalankhula naye m’maloto.+

  • Yobu 33:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Iye amawalankhula m’maloto+ ndi m’masomphenya+ a usiku,

      Anthu akakhala m’tulo tofa nato,

      Akamagona pabedi.+

  • Yeremiya 23:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Mneneri amene walota maloto anene maloto akewo. Koma amene ndamuuza mawu anga, alankhule mawu angawo moona.”+

      “Kodi mapesi a tirigu angafanane ndi tirigu weniweniyo?”+ watero Yehova.

  • Danieli 2:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Ndiyeno usiku, chinsinsicho chinaululidwa kwa Danieli m’masomphenya.+ Pamenepo Danieli anatamanda+ Mulungu wakumwamba.

  • Danieli 8:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 M’chaka chachitatu cha ulamuliro wa mfumu Belisazara,+ ineyo Danieli ndinaona masomphenya pambuyo pa masomphenya amene ndinaona poyambirira aja.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena