Yeremiya 51:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Babulo wakhala kapu yagolide m’dzanja la Yehova+ ndipo waledzeretsa dziko lonse lapansi.+ Mitundu ya anthu yaledzera ndi vinyo wake.+ N’chifukwa chake mitundu ya anthu ikuchita zinthu zamisala.+ Danieli 2:38 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 38 inuyo amene Mulungu wakupatsani+ nyama zakutchire ndi mbalame zam’mlengalenga kulikonse kumene kuli anthu, amene Mulungu wakuikani kukhala wolamulira zonsezo, inuyo ndiye mutu wagolide.+ Danieli 4:22 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 22 Mtengowo ndinuyo mfumu,+ chifukwa mwakula ndipo mwakhala ndi mphamvu. Ulemerero wanu wakula mpaka kufika kumwamba+ ndipo ulamuliro wanu wafika kumalekezero a dziko lapansi.+ Danieli 7:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 “Chilombo choyamba chinali chooneka ngati mkango+ ndipo chinali ndi mapiko a chiwombankhanga.+ Ndinapitiriza kuchiyang’ana kufikira pamene mapiko ake anathotholedwa. Ndiyeno anachitukula padziko lapansi+ ndipo anachiimiritsa ndi miyendo iwiri ngati munthu. Kenako chinapatsidwa mtima wa munthu.+
7 Babulo wakhala kapu yagolide m’dzanja la Yehova+ ndipo waledzeretsa dziko lonse lapansi.+ Mitundu ya anthu yaledzera ndi vinyo wake.+ N’chifukwa chake mitundu ya anthu ikuchita zinthu zamisala.+
38 inuyo amene Mulungu wakupatsani+ nyama zakutchire ndi mbalame zam’mlengalenga kulikonse kumene kuli anthu, amene Mulungu wakuikani kukhala wolamulira zonsezo, inuyo ndiye mutu wagolide.+
22 Mtengowo ndinuyo mfumu,+ chifukwa mwakula ndipo mwakhala ndi mphamvu. Ulemerero wanu wakula mpaka kufika kumwamba+ ndipo ulamuliro wanu wafika kumalekezero a dziko lapansi.+
4 “Chilombo choyamba chinali chooneka ngati mkango+ ndipo chinali ndi mapiko a chiwombankhanga.+ Ndinapitiriza kuchiyang’ana kufikira pamene mapiko ake anathotholedwa. Ndiyeno anachitukula padziko lapansi+ ndipo anachiimiritsa ndi miyendo iwiri ngati munthu. Kenako chinapatsidwa mtima wa munthu.+