Yesaya 13:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Pakuti nyenyezi zakumwamba ndi magulu a nyenyezi a Kesili+ sizidzawala. Dzuwa lidzachita mdima potuluka, ndipo mwezi sudzaonetsa kuwala kwake. Ezekieli 32:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 “‘Ndikadzakuzimitsa, ndidzaphimba kumwamba n’kuchititsa mdima nyenyezi zake. Dzuwa ndidzaliphimba ndi mitambo ndipo mwezi sudzaonetsa kuwala kwake.+ Yoweli 2:31 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 31 Dzuwa lidzasanduka mdima,+ ndipo mwezi udzasanduka magazi.+ Zimenezi zidzachitika tsiku lalikulu ndi lochititsa mantha la Yehova lisanafike.+ Machitidwe 2:20 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 20 Dzuwa+ lidzasanduka mdima, ndipo mwezi udzasanduka magazi. Zimenezi zidzachitika tsiku lalikulu ndi laulemerero la Yehova* lisanafike.+
10 Pakuti nyenyezi zakumwamba ndi magulu a nyenyezi a Kesili+ sizidzawala. Dzuwa lidzachita mdima potuluka, ndipo mwezi sudzaonetsa kuwala kwake.
7 “‘Ndikadzakuzimitsa, ndidzaphimba kumwamba n’kuchititsa mdima nyenyezi zake. Dzuwa ndidzaliphimba ndi mitambo ndipo mwezi sudzaonetsa kuwala kwake.+
31 Dzuwa lidzasanduka mdima,+ ndipo mwezi udzasanduka magazi.+ Zimenezi zidzachitika tsiku lalikulu ndi lochititsa mantha la Yehova lisanafike.+
20 Dzuwa+ lidzasanduka mdima, ndipo mwezi udzasanduka magazi. Zimenezi zidzachitika tsiku lalikulu ndi laulemerero la Yehova* lisanafike.+