Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 36:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Ndiyeno m’chaka chachisanu cha ulamuliro wa Yehoyakimu+ mwana wa Yosiya, mfumu ya Yuda, m’mwezi wa 9,+ analengeza kuti anthu onse a mu Yerusalemu ndi anthu onse amene anali kubwera ku Yerusalemu kuchokera m’mizinda ya Yuda asale kudya pamaso pa Yehova.+

  • Yoweli 1:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Konzekerani nthawi yosala kudya.+ Itanitsani msonkhano wapadera.+ Sonkhanitsani pamodzi akulu ndi anthu onse okhala m’dzikoli kuti akumane kunyumba ya Yehova Mulungu wanu+ ndipo alirire Yehova kuti awathandize.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena