Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 9:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 dziwa kuti, dzanja la Yehova+ lipha ziweto zanu zonse.+ Mliri waukulu kwambiri ugwera mahatchi,* abulu, ngamila, ng’ombe ndi nkhosa.+

  • Deuteronomo 28:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 “Yehova adzakulanga ndi zithupsa za ku Iguputo,+ matenda a mudzi,* ziwengo ndi zotupa, ndipo sudzachira matenda amenewa.

  • Deuteronomo 28:60
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 60 Adzakubweretsera matenda onse a ku Iguputo amene unachita nawo mantha, ndipo adzakumamatira.+

  • Salimo 78:50
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 50 Mkwiyo wake anaulambulira njira.+

      Sanawabweze kuwachotsa ku imfa.

      Ndipo anawapha ndi mliri.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena