Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 16:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Kunyada kumafikitsa munthu ku chiwonongeko,+ ndipo mtima wodzikuza umachititsa munthu kupunthwa.+

  • Yeremiya 49:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Iwe unachititsa anthu kunjenjemera ndiponso unali ndi mtima wodzikuza,+ koma zimenezi zakunyenga, iwe amene ukukhala m’malo obisika a m’thanthwe pamwamba pa phiri. Ngakhale kuti umamanga chisa chako pamwamba kwambiri ngati chiwombankhanga+ ndidzakugwetsa kuchoka pamenepo,”+ watero Yehova.

  • Malaki 1:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 “Popeza kuti Edomu akunena kuti, ‘Ife tawonongedwa, koma tibwerera ndi kukamanga malo athu owonongedwawo,’ Yehova wa makamu wanena kuti, ‘Iwo akamanga, koma ine ndikagwetsa.+ Anthu adzatcha malo awowo, “dera la zoipa” ndipo iwowo adzatchedwa, “anthu okanidwa ndi Yehova+ mpaka kalekale.”*

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena