-
Luka 10:21Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
21 Nthawi yomweyo Yesu anakondwera+ kwambiri mwa mzimu woyera n’kunena kuti: “Atate ndikukutamandani pamaso pa onse, inu Ambuye wakumwamba ndi dziko lapansi, chifukwa zinthu izi mwazibisa kwa anzeru+ ndi ozama m’maphunziro, koma mwaziulula kwa tiana. Inde Atate, chifukwa inu munakonda kuti zinthu zikhale chonchi.
-