Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 9:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Pamene Yesu anali kudutsa kuchokera kumeneko, anthu awiri akhungu+ anam’tsatira. Iwo anafuula ndi kunena kuti: “Mutichitire chifundo,+ Mwana wa Davide.”

  • Mateyu 15:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Ndiyeno kunabwera mayi wina wa ku Foinike+ kuchokera m’zigawo zimenezo ndi kufuula kuti: “Ndichitireni chifundo+ Ambuye, Mwana wa Davide. Mwana wanga wamkazi wagwidwa ndi chiwanda mochititsa mantha.”

  • Maliko 10:47
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 47 Pamene anamva kuti ndi Yesu Mnazareti, Batimeyu anayamba kufuula kuti: “Mwana wa Davide,+ Yesu, ndichitireni chifundo!”+

  • Luka 18:38
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 38 Atamva zimenezo anafuula kuti: “Yesu, Mwana wa Davide, ndichitireni chifundo!”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena