Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 9:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Atatulutsa anthu aja panja, iye analowa ndi kugwira dzanja la mtsikanayo,+ ndipo iye anadzuka.+

  • Luka 7:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Atatero anayandikira ndi kugwira chithathacho. Pamenepo onyamulawo anangoima chilili, ndipo iye anati: “Mnyamata iwe, ndikunena ndi iwe, Dzuka!”+

  • Luka 8:54
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 54 Koma iye anamugwira dzanja ndi kuitana kuti: “Mtsikana iwe, dzuka!”+

  • Machitidwe 9:40
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 40 Koma Petulo anatulutsa anthu onse,+ ndiyeno anagwada pansi ndi kupemphera. Kenako anatembenukira mtembowo ndi kunena kuti: “Tabita, dzuka!” Pamenepo mayiyo anatsegula maso ake, ndipo mmene anaona Petulo, anadzuka n’kukhala tsonga.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena