Mateyu 9:20 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 20 Tsopano mayi wina amene anali ndi nthenda yotaya magazi kwa zaka 12+ anafika kumbuyo kwake n’kugwira ulusi wopota wa m’mphepete mwa malaya ake akunja,+ Maliko 5:27 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 27 Atamva zambiri zokhudza Yesu, anakalowa m’khamu la anthulo ndi kumudzera kumbuyo kwake, kenako anagwira+ malaya ake akunja. Luka 8:44 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 44 Mayiyu anamudzera kumbuyo Yesu n’kugwira ulusi wopota wa m’mphepete+ mwa malaya ake akunja.+ Nthawi yomweyo anasiya kutaya magazi.+ Machitidwe 19:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Moti anthu anali kutenga ngakhale mipango yopukutira thukuta ndi maepuloni amene akhudza thupi la Paulo n’kupita nazo kwa odwala,+ ndipo matenda awo anali kutheratu. Mizimu yoipa nayonso inali kutuluka.+
20 Tsopano mayi wina amene anali ndi nthenda yotaya magazi kwa zaka 12+ anafika kumbuyo kwake n’kugwira ulusi wopota wa m’mphepete mwa malaya ake akunja,+
27 Atamva zambiri zokhudza Yesu, anakalowa m’khamu la anthulo ndi kumudzera kumbuyo kwake, kenako anagwira+ malaya ake akunja.
44 Mayiyu anamudzera kumbuyo Yesu n’kugwira ulusi wopota wa m’mphepete+ mwa malaya ake akunja.+ Nthawi yomweyo anasiya kutaya magazi.+
12 Moti anthu anali kutenga ngakhale mipango yopukutira thukuta ndi maepuloni amene akhudza thupi la Paulo n’kupita nazo kwa odwala,+ ndipo matenda awo anali kutheratu. Mizimu yoipa nayonso inali kutuluka.+