Deuteronomo 33:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Iye analinso kukonda anthu ake.+Oyera awo onse ali m’manja mwanu.+Iwowa anakhala pansi, pamapazi panu.+Anayamba kulandira ena mwa mawu anu.+ Luka 8:35 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 35 Zitatero anthu anabwera kudzaona zomwe zachitikazo. Atafika kwa Yesu anapeza munthu amene anam’tulutsa ziwanda uja atakhala pansi pafupi ndi Yesu. Anamupeza atavala bwino komanso maganizo ake ali bwinobwino, ndipo iwo anachita mantha.+ Machitidwe 22:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 “Inetu ndine Myuda,+ wobadwira ku Tariso wa ku Kilikiya,+ koma ndinaphunzitsidwa ndi Gamaliyeli+ mumzinda womwe uno. Anandiphunzitsa kutsatira Chilamulo cha makolo athu mokhwimitsa zinthu kwambiri.+ Ndipo ndinali wodzipereka+ potumikira Mulungu monga mmene nonsenu mulili lero.
3 Iye analinso kukonda anthu ake.+Oyera awo onse ali m’manja mwanu.+Iwowa anakhala pansi, pamapazi panu.+Anayamba kulandira ena mwa mawu anu.+
35 Zitatero anthu anabwera kudzaona zomwe zachitikazo. Atafika kwa Yesu anapeza munthu amene anam’tulutsa ziwanda uja atakhala pansi pafupi ndi Yesu. Anamupeza atavala bwino komanso maganizo ake ali bwinobwino, ndipo iwo anachita mantha.+
3 “Inetu ndine Myuda,+ wobadwira ku Tariso wa ku Kilikiya,+ koma ndinaphunzitsidwa ndi Gamaliyeli+ mumzinda womwe uno. Anandiphunzitsa kutsatira Chilamulo cha makolo athu mokhwimitsa zinthu kwambiri.+ Ndipo ndinali wodzipereka+ potumikira Mulungu monga mmene nonsenu mulili lero.