Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 71:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Chilungamo chanu, inu Mulungu chafika kumwamba.+

      Tikanena za zinthu zazikulu zimene munachita,+

      Inu Mulungu, ndani angafanane ndi inu?+

  • Salimo 111:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Wawombola anthu ake.+

      צ [Tsa·dhehʹ]

      Wakhazikitsa pangano lake mpaka kalekale.+

      ק [Qohph]

      Dzina lake ndi loyera ndi lochititsa mantha.+

  • Yesaya 57:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Pakuti Wapamwamba ndi Wokwezeka,+ yemwe adzakhalepo kwamuyaya+ ndiponso yemwe dzina lake ndi loyera,+ wanena kuti: “Ine ndimakhala kumwamba pamalo oyera.+ Ndimakhalanso ndi munthu wopsinjika ndi wa mtima wodzichepetsa,+ kuti nditsitsimutse mtima wa anthu onyozeka ndiponso kuti nditsitsimutse mtima wa anthu opsinjika.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena