Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 9:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Nthawi inayake, pamene anali kudya patebulo m’nyumba ina,+ kunabwera okhometsa msonkho ndi ochimwa ambiri ndipo anayamba kudya pamodzi ndi Yesu ndi ophunzira ake.

  • Maliko 2:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Pa nthawi ina Yesu anali kudya patebulo m’nyumba ya Levi, ndipo okhometsa msonkho+ ndi ochimwa ambiri anali kudya pamodzi ndi iye ndi ophunzira ake. Kumeneko kunali anthu ambiri ndipo anayamba kumutsatira.+

  • Luka 5:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Tsopano Levi anakonzera Yesu phwando lalikulu kunyumba kwake. Kumeneko kunali khamu lalikulu la okhometsa msonkho ndi ena ambiri, ndipo anali kudyera limodzi.+

  • Luka 19:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Kumeneko kunali munthu wina dzina lake Zakeyu. Iyeyu anali mkulu wa okhometsa msonkho, ndipo anali wolemera.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena