Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 37:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Woipa amalondalonda munthu wolungama,+

      Ndipo amafuna kuti amuphe.+

  • Miyambo 1:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Chifukwa mapazi awo amathamangira zoipa,+ ndipo iwo amafulumira kukakhetsa magazi.+

  • Machitidwe 9:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Tsopano patapita masiku ambiri, Ayudawo anasonkhana pamodzi ndi kupangana zoti amuphe.+

  • Machitidwe 14:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Ndiyeno anthu a mitundu ina komanso Ayuda pamodzi ndi olamulira awo, anakonza chiwembu kuti achitire chipongwe atumwiwo ndi kuwaponya miyala.+

  • Machitidwe 23:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Koma chonde musalole kuti akunyengerereni, pakuti amuna oposa 40 akumudikirira panjira.+ Amenewa achita kulumbira modzitemberera kuti sadya kapena kumwa kanthu kufikira atamupha.+ Moti panopa akonzeka, akungoyembekezera chilolezo chanu.”

  • 2 Akorinto 11:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Pa maulendo kawirikawiri, zoopsa za m’mitsinje, zoopsa za achifwamba pamsewu,+ zoopsa zochokera kwa anthu a mtundu wanga,+ zoopsa zochokera kwa anthu a mitundu ina,+ zoopsa mumzinda,+ zoopsa m’chipululu, zoopsa za panyanja, zoopsa pakati pa abale onyenga,

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena