Danieli 6:16 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 16 Zitatero mfumuyo inalamula kuti abweretse Danieli. Atabwera naye anamuponya m’dzenje la mikango.+ Koma mfumu inauza Danieli kuti: “Mulungu wako amene umamutumikira mosalekeza akupulumutsa.”+ Machitidwe 5:19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 Koma usiku, mngelo wa Yehova+ anatsegula zitseko za ndendeyo+ ndi kuwatulutsa, ndipo anawauza kuti: Machitidwe 23:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Koma tsiku lomwelo usiku, Ambuye anaimirira pambali pake+ ndi kunena kuti: “Limba mtima!+ Pakuti wandichitira umboni mokwanira+ mu Yerusalemu, ndipo ukandichitiranso umboni ku Roma.”+ Aheberi 1:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Kodi angelo onse si mizimu+ yotumikira ena,+ yotumidwa kukatumikira amene adzalandire chipulumutso monga cholowa chawo?+
16 Zitatero mfumuyo inalamula kuti abweretse Danieli. Atabwera naye anamuponya m’dzenje la mikango.+ Koma mfumu inauza Danieli kuti: “Mulungu wako amene umamutumikira mosalekeza akupulumutsa.”+
19 Koma usiku, mngelo wa Yehova+ anatsegula zitseko za ndendeyo+ ndi kuwatulutsa, ndipo anawauza kuti:
11 Koma tsiku lomwelo usiku, Ambuye anaimirira pambali pake+ ndi kunena kuti: “Limba mtima!+ Pakuti wandichitira umboni mokwanira+ mu Yerusalemu, ndipo ukandichitiranso umboni ku Roma.”+
14 Kodi angelo onse si mizimu+ yotumikira ena,+ yotumidwa kukatumikira amene adzalandire chipulumutso monga cholowa chawo?+