Levitiko 27:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Koma ngati wolonjezayo ndi wosauka moti sangakwanitse mtengo woikidwiratuwo,+ azikaonetsa munthu woperekedwayo kwa wansembe, ndipo wansembe azinena mtengo wa munthuyo.+ Wansembe adzanena mtengo umene wolonjezayo angakwanitse.+ Deuteronomo 16:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Ndiyeno uzichitira Yehova Mulungu wako+ chikondwerero cha masabata, popereka nsembe zaufulu zimene ungathe, monga mmene Yehova Mulungu wako angakudalitsire.+ Deuteronomo 16:17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 17 Mphatso yochokera m’manja mwa aliyense izikhala yolingana ndi madalitso amene Yehova Mulungu wanu wakupatsani.+ Miyambo 3:27 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 27 Usalephere kuchitira zabwino anthu amene akufunikira zabwinozo,+ pamene dzanja lako lingathe kuchita zimenezo.+ Maliko 12:43 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 43 Choncho Yesu anaitana ophunzira ake ndi kuwauza kuti: “Ndithu ndikukuuzani, mkazi wamasiye wosaukayu waponya zochuluka kuposa onse amene aponya ndalama moponya zoperekamo.+ Luka 21:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Ndipo iye anati: “Kunena zoona, Mkazi wamasiyeyu, ngakhale kuti ndi wosauka, waponya zochuluka kuposa onse amene aponya.+
8 Koma ngati wolonjezayo ndi wosauka moti sangakwanitse mtengo woikidwiratuwo,+ azikaonetsa munthu woperekedwayo kwa wansembe, ndipo wansembe azinena mtengo wa munthuyo.+ Wansembe adzanena mtengo umene wolonjezayo angakwanitse.+
10 Ndiyeno uzichitira Yehova Mulungu wako+ chikondwerero cha masabata, popereka nsembe zaufulu zimene ungathe, monga mmene Yehova Mulungu wako angakudalitsire.+
17 Mphatso yochokera m’manja mwa aliyense izikhala yolingana ndi madalitso amene Yehova Mulungu wanu wakupatsani.+
27 Usalephere kuchitira zabwino anthu amene akufunikira zabwinozo,+ pamene dzanja lako lingathe kuchita zimenezo.+
43 Choncho Yesu anaitana ophunzira ake ndi kuwauza kuti: “Ndithu ndikukuuzani, mkazi wamasiye wosaukayu waponya zochuluka kuposa onse amene aponya ndalama moponya zoperekamo.+
3 Ndipo iye anati: “Kunena zoona, Mkazi wamasiyeyu, ngakhale kuti ndi wosauka, waponya zochuluka kuposa onse amene aponya.+