Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 124:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Moyo wathu uli ngati mbalame imene yathawa+

      Pamsampha wa munthu wogwiritsa ntchito nyambo.+

      Msamphawo wathyoka,+

      Ndipo ife tapulumuka.+

  • Yohane 13:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Atamupatsa chidutswa cha mkatecho, pamenepo Satana analowa mwa Yudasi.+ Chotero Yesu anamuuza kuti: “Zimene wakonza kuchita, zichite mwamsanga.”

  • Machitidwe 5:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Koma Petulo anati: “Hananiya, n’chifukwa chiyani Satana+ wakulimbitsa mtima choncho kuti uyese kunamiza+ mzimu woyera+ ndi kubisa zina mwa ndalama za mtengo wa mundawo?

  • 1 Timoteyo 1:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Ena mwa amenewa ndi Hemenayo+ ndi Alekizanda,+ ndipo ndawapereka kwa Satana+ kuti akalangidwa,* aphunzire kuti sayenera kulankhula zonyoza Mulungu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena