Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 21:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Aliyense wotseka khutu lake kuti asamve kudandaula kwa munthu wonyozeka,+ nayenso adzaitana koma sadzayankhidwa.+

  • Yesaya 3:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Tsoka kwa anthu oipa! Iwo adzaona zoopsa, chifukwa zimene anachitira ena ndi manja awo, zidzawachitikira iwowo.+

  • Mateyu 5:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 “Odala ndi anthu achifundo,+ chifukwa adzachitiridwa chifundo.

  • Mateyu 6:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Koma ngati simukhululukira anthu machimo awo, Atate wanu sadzakukhululukirani machimo anu.+

  • Luka 6:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Pitirizani kukhala achifundo, potengera Atate wanu amenenso ali wachifundo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena