Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 5/15 tsamba 4
  • Zitsanzo za Ulaliki

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zitsanzo za Ulaliki
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Nkhani Yofanana
  • Zomwe Munganene Pogawira Magazini
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
Onani Zambiri
Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
km 5/15 tsamba 4

Zitsanzo za Ulaliki

Nsanja ya Olonda June 1

“Tikucheza ndi anthu a m’dera lino ndipo tikukambirana nawo kufunika kwa Baibulo. Ambiri amaona kuti sayansi ikupangitsa anthu kumaona kuti Baibulo si lolondola. Kodi inuyo mukuganiza bwanji? Kodi mukuona kuti tiyenera kukhulupirira Baibulo? [Yembekezerani ayankhe.] Taonani chitsanzo chimodzi chosonyeza kuti Baibulo ndi lolondola. [Werengani Yobu 26:7.] Magaziniyi ikufotokoza kugwirizana kwa zimene Baibulo limanena ndi zimene asayansi apeza.”

Galamukani! June

“Popeza masiku ano anthu ambiri akuvutika ndi matenda, tikukambirana ndi anthu vesi lolimbikitsa la m’Baibulo ili. [Werengani Yesaya 33:24a.] Kodi mukuganiza kuti moyo wathu ukanakhala wotani tikanakhala kuti sitidwala? [Yembekezerani ayankhe.] Posachedwapa ulosi umenewu ukwaniritsidwa. Komabe magaziniyi ikufotokoza mfundo 5 zomwe zingatithandize kuti tikhale ndi moyo wathanzi panopa.”

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena