Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 10/15 tsamba 4
  • Zitsanzo za Ulaliki

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zitsanzo za Ulaliki
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Nkhani Yofanana
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
Onani Zambiri
Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
km 10/15 tsamba 4

Zitsanzo za Ulaliki

Nsanja ya Olonda November 1

“Magulu awiri akayamba kumenyana, mbali iliyonse imaganiza kuti Mulungu akuwathandiza. Koma kodi Mulungu amavomereza zoti anthu azimenya nkhondo? [Yembekezerani ayankhe.] Magaziniyi ikufotokoza chifukwa chake Mulungu ankamenya nkhondo kale. Ikufotokozanso zimene adzachite posachedwapa, zomwe zidzathetseretu nkhondo padzikoli.” Werengani Salimo 46:9 ndipo kenako apatseni magaziniwo.

Galamukani! November

“Anthu ambiri padzikoli amakhumudwa chifukwa cha chinyengo komanso zinthu zabodza zomwe zipembedzo zosiyanasiyana zimaphunzitsa. Kodi mukuganiza kuti zipembedzo zili ndi tsogolo lotani? [Yembekezerani ayankhe.] Magaziniyi ikufotokoza ulosi wochititsa chidwi wa m’buku la Chivumbulutso umene unaneneratu kuti m’nthawi yathu ino anthu ambiri adzatuluka m’chipembedzo chonyenga. Ulosiwu umasonyezanso kuti posachedwapa zipembedzo zonse zonyenga ziwonongedwa.”

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena