Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 11/15 tsamba 4
  • Zitsanzo za Ulaliki

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zitsanzo za Ulaliki
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Nkhani Yofanana
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Zomwe Munganene Pogawira Magazini
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
Onani Zambiri
Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
km 11/15 tsamba 4

Zitsanzo za Ulaliki

Nsanja ya Olonda December 1

“Anthu ambiri amakhala ndi maganizo olakwika pa nkhani ya Baibulo. N’zoona kuti amalilemekeza koma amaona kuti ndi lovuta kulimvetsa. Inuyo mumaliona bwanji? [Yembekezerani ayankhe.] Tiyeni tiwerenge Aroma 15:4 kuti tione chifukwa chake tiyenera kumvetsa Baibulo. [Werengani.] Magaziniyi ikusonyeza kuti Baibulo linalembedwa m’njira yoti tizilimvetsa komanso ikufotokoza zimene tingachite kuti tizilimvetsa.”

Galamukani! December

“Tikukambirana ndi anthu nkhani yothandiza kwambiri mabanja. Aliyense amafuna kuti azikhala mwamtendere m’banja. Kodi n’zotheka kuti anthu m’banja asamasiyane maganizo? Ngati n’zosatheka, kodi tingatani kuti tizithetsa bwino kusiyana maganizo? [Yembekezerani ayankhe.] Tiyeni tione zimene Baibulo limanena pa Miyambo 26:20. [Werengani.] Magaziniyi ikufotokoza malangizo opezeka m’Baibulo amene angathandize mabanja kukhala mwamtendere.”

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena