Ekisodo 7:22 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 22 Komano, ansembe ochita zamatsenga a ku Iguputo anachitanso zomwezo mwa matsenga awo,+ moti Farao anaumitsabe mtima wake,+ ndipo sanamvere Mose ndi Aroni, monga Yehova ananenera.+ Ekisodo 8:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 Ndipo ansembe ochita zamatsenga, anafunanso kuti apange ntchentche zoluma mwa matsenga awo,+ koma analephera.+ Ndipo ntchentchezo zinali kuluma anthu ndi nyama zomwe. Ekisodo 9:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Ndipo ansembe ochita zamatsenga sanathe kuonekera pamaso pa Mose chifukwa cha zithupsazo, popeza zinatuluka pa ansembewo ndi pa Aiguputo onse.+ Machitidwe 8:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Tsopano mumzindawo munalinso munthu wina dzina lake Simoni. Izi zisanachitike, iyeyu anali kuchita zamatsenga+ ndi kudabwitsa anthu onse mu Samariya. Anali kudzitamandira kuti anali wopambana.+ 2 Atesalonika 2:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Koma kukhalapo kwa wosamvera malamuloyo kukutheka mwa mphamvu+ za Satana. Adzachita ntchito iliyonse yamphamvu ndi zizindikiro zabodza ndi zodabwitsa,+
22 Komano, ansembe ochita zamatsenga a ku Iguputo anachitanso zomwezo mwa matsenga awo,+ moti Farao anaumitsabe mtima wake,+ ndipo sanamvere Mose ndi Aroni, monga Yehova ananenera.+
18 Ndipo ansembe ochita zamatsenga, anafunanso kuti apange ntchentche zoluma mwa matsenga awo,+ koma analephera.+ Ndipo ntchentchezo zinali kuluma anthu ndi nyama zomwe.
11 Ndipo ansembe ochita zamatsenga sanathe kuonekera pamaso pa Mose chifukwa cha zithupsazo, popeza zinatuluka pa ansembewo ndi pa Aiguputo onse.+
9 Tsopano mumzindawo munalinso munthu wina dzina lake Simoni. Izi zisanachitike, iyeyu anali kuchita zamatsenga+ ndi kudabwitsa anthu onse mu Samariya. Anali kudzitamandira kuti anali wopambana.+
9 Koma kukhalapo kwa wosamvera malamuloyo kukutheka mwa mphamvu+ za Satana. Adzachita ntchito iliyonse yamphamvu ndi zizindikiro zabodza ndi zodabwitsa,+