-
Genesis 14:20Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
Pamenepo, Abulamu anamupatsa iye chakhumi cha zilizonse.+
-
-
Malaki 3:10Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
10 Bweretsani gawo limodzi mwa magawo 10 alionse a zinthu zanu+ n’kuziika mosungiramo zinthu zanga, kuti m’nyumba mwanga mukhale chakudya.+ Ndiyeseni chonde pa nkhani imeneyi,+ kuti muone ngati sindidzakutsegulirani zipata za kumwamba+ ndi kukukhuthulirani madalitso oti mudzasowa powalandirira,”+ watero Yehova wa makamu.
-