31 Kenako azichotsa mafuta onse+ a mbuziyo, monga mmene amachotsera mafuta a nsembe yachiyanjano.+ Pamenepo wansembe azitentha mafutawo paguwa lansembe kuti likhale fungo lokhazika mtima pansi kwa Yehova.+ Ndiyeno wansembe aziphimba tchimo la munthuyo, ndipo azikhululukidwa.+