Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 32:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Iwo anali kupereka nsembe kwa ziwanda, osati kwa Mulungu.+

      Anapereka nsembe kwa milungu imene sanaidziwe,+

      Milungu yatsopano yongobwera kumene,+

      Imene makolo anu akale sanaidziwe.

  • Yoswa 24:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 “Tsopano opani Yehova+ ndi kum’tumikira mosalakwitsa ndiponso mokhulupirika.*+ Chotsani milungu imene makolo anu ankatumikira kutsidya lina la Mtsinje ndi ku Iguputo,+ ndipo tumikirani Yehova.

  • 2 Mbiri 11:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Iye anadziikira ansembe m’malo okwezeka+ kuti azitumikira ziwanda zooneka ngati mbuzi*+ ndi mafano a ana a ng’ombe amene iye anapanga.+

  • 1 Akorinto 10:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Ayi, koma ndikunena kuti zinthu zimene mitundu ina imapereka nsembe imazipereka kwa ziwanda,+ osati kwa Mulungu, ndipo sindikufuna kuti mukhale ogawana ndi ziwanda.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena