Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 24:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Patapita nthawi, ndinatumiza Mose ndi Aroni,+ ndipo ndinagwetsera Iguputo miliri.+ Nditatero ndinakutulutsani+ ku Iguputoko.

  • 1 Samueli 12:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 “Yakobo atangofika mu Iguputo,+ makolo anu n’kuyamba kupempha thandizo+ kwa Yehova, Yehova anatumiza Mose+ ndi Aroni kuti atsogolere makolo anu potuluka mu Iguputo, ndipo anawapatsa dziko lino kuti akhalemo.+

  • Salimo 77:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Mwatsogolera anthu anu ngati nkhosa,+

      Kudzera mwa Mose ndi Aroni.+

  • Mika 6:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ine ndinakutulutsani m’dziko la Iguputo,+ ndipo ndinakuwombolani m’nyumba ya akapolo.+ Ndinakutumizirani Mose, Aroni ndi Miriamu kuti akutsogolereni.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena