8 “Yakobo atangofika mu Iguputo,+ makolo anu n’kuyamba kupempha thandizo+ kwa Yehova, Yehova anatumiza Mose+ ndi Aroni kuti atsogolere makolo anu potuluka mu Iguputo, ndipo anawapatsa dziko lino kuti akhalemo.+
4 Ine ndinakutulutsani m’dziko la Iguputo,+ ndipo ndinakuwombolani m’nyumba ya akapolo.+ Ndinakutumizirani Mose, Aroni ndi Miriamu kuti akutsogolereni.+