Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 30:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 “Koma iwe udzatembenuka ndi kumvera mawu a Yehova ndi kutsatira malamulo ake onse amene ndikukupatsa lero.+

  • Yoswa 22:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Koma mukaonetsetse kuti mukusunga malamulo+ ndi Chilamulo chimene Mose mtumiki wa Yehova anakulamulirani. Mukachite zimenezi mwa kukonda Yehova Mulungu wanu,+ kuyenda m’njira zake zonse,+ kusunga malamulo ake,+ kum’mamatira,+ ndiponso kum’tumikira+ ndi mtima wanu wonse+ ndiponso moyo wanu wonse.”+

  • Mlaliki 12:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Poti zonse zanenedwa, mfundo yaikulu ndi yakuti: Opa Mulungu woona+ ndi kusunga malamulo ake+ chifukwa zimenezi ndiye zimene munthu ayenera kuchita.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena