Levitiko 10:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 “Pamene mukubwera kuchihema chokumanako, iwe ndi ana ako musamamwe vinyo kapena zakumwa zina zoledzeretsa,+ kuti mungafe. Limeneli ndi lamulo ku mibadwo yanu yonse mpaka kalekale, Oweruza 13:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Asadye chilichonse chochokera ku mphesa zopangira vinyo, asamwe vinyo+ kapena chakumwa chilichonse choledzeretsa, ndipo asadye chilichonse chodetsedwa.+ Asunge zonse zimene ndamuuza.”+ Amosi 2:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 “‘Koma inu munapitiriza kupatsa Anaziri vinyo kuti amwe+ ndipo aneneri munawalamula kuti: “Musamanenere.”+ Luka 1:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 chifukwa adzakhala wamkulu pamaso pa Yehova.+ Koma asadzamwe vinyo ngakhale pang’ono+ kapena chakumwa chaukali chilichonse. Ndipo adzadzazidwa ndi mzimu woyera kuyambira ali m’mimba mwa mayi ake.+ Luka 7:33 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 33 Mofanana ndi zimenezi, Yohane M’batizi anabwera ndipo sadya chakudya kapena kumwa vinyo, koma inu mumanena kuti, ‘Ali ndi chiwanda.’+
9 “Pamene mukubwera kuchihema chokumanako, iwe ndi ana ako musamamwe vinyo kapena zakumwa zina zoledzeretsa,+ kuti mungafe. Limeneli ndi lamulo ku mibadwo yanu yonse mpaka kalekale,
14 Asadye chilichonse chochokera ku mphesa zopangira vinyo, asamwe vinyo+ kapena chakumwa chilichonse choledzeretsa, ndipo asadye chilichonse chodetsedwa.+ Asunge zonse zimene ndamuuza.”+
12 “‘Koma inu munapitiriza kupatsa Anaziri vinyo kuti amwe+ ndipo aneneri munawalamula kuti: “Musamanenere.”+
15 chifukwa adzakhala wamkulu pamaso pa Yehova.+ Koma asadzamwe vinyo ngakhale pang’ono+ kapena chakumwa chaukali chilichonse. Ndipo adzadzazidwa ndi mzimu woyera kuyambira ali m’mimba mwa mayi ake.+
33 Mofanana ndi zimenezi, Yohane M’batizi anabwera ndipo sadya chakudya kapena kumwa vinyo, koma inu mumanena kuti, ‘Ali ndi chiwanda.’+