Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 3:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Atafika kumeneko anayamba kuliza lipenga la nyanga+ ya nkhosa m’dera lamapiri la Efuraimu.+ Iye ali patsogolo, ana a Isiraeli anatsika naye limodzi kuchoka m’dera lamapirilo.

  • Oweruza 7:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Ndipo magulu atatuwo analiza malipenga a nyanga ya nkhosa+ ndi kuphwanya mitsuko ikuluikulu ija. Atatero ananyamulanso miyuni ndi dzanja lawo lamanzere ndipo malipenga anali m’dzanja lawo lamanja, n’kuyamba kufuula kuti: “Nkhondo ya Yehova+ ndi ya Gidiyoni!”

  • 2 Mbiri 13:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Taonani, ife patsogolo pathu pali Mulungu woona+ ndi ansembe ake,+ ndi malipenga+ otiitanira ku nkhondo yomenyana nanu. Inu ana a Isiraeli, musamenyane ndi Yehova Mulungu wa makolo anu,+ chifukwa simupambana.”+

  • 1 Akorinto 14:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Ndithudi, ngati lipenga likulira mwa mamvekedwe osadziwika bwino, ndani angakonzekere nkhondo?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena