Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 10:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Atatero Mose anauza Aroni ndi ana ake ena, Eleazara ndi Itamara, kuti: “Musalekerere tsitsi lanu osalisamala,+ ndipo musang’ambe zovala zanu kuti mungafe ndiponso kuti Mulungu angakwiyire khamu lonseli.+ Abale anu, nyumba yonse ya Isiraeli ndiwo alire chifukwa cha kuwononga ndi moto kumene Yehova wachita.

  • Numeri 8:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Ndipo ndidzapereka Alevi kwa Aroni ndi ana ake monga operekedwa kuchokera mwa ana a Isiraeli.+ Aleviwo adzatumikira m’malo mwa ana a Isiraeli pachihema chokumanako,+ ndipo aziphimba machimo a ana a Isiraeli.+ Chifukwa cha utumiki wawowo, mliri sudzawagwera ana a Isiraeli pakuti sadzayandikira malo oyerawo.”

  • Numeri 16:46
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 46 Kenako Mose anauza Aroni kuti: “Tenga chofukizira uikemo moto wochokera paguwa lansembe.+ Uikemo nsembe yofukiza n’kupita kwa khamulo mofulumira kuti ukawaphimbire machimo awo.+ Chita zimenezi chifukwa Yehova wakwiya kwambiri.+ Mliritu wayamba kale!”

  • Numeri 18:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Muzichita utumiki wanu m’malo oyera+ ndi paguwa lansembe,+ kuti mkwiyo+ usadzawabukirenso ana a Isiraeli.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena