-
Oweruza 20:10Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
10 Ndipo m’mafuko onse a Isiraeli titengemo amuna 10 mwa amuna 100 alionse, amuna 100 mwa amuna 1,000 alionse, amuna 1,000 mwa amuna 10,000 alionse. Amenewa azipezera anthu zofunika, kuti anthuwo achitepo kanthu mwa kupita ndi kukamenyana ndi Gibeya wa ku Benjamini, chifukwa cha chinthu chochititsa manyazi ndi chopusa+ chimene achita mu Isiraeli.”
-