Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 22:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Udzamudandaulira ndipo adzakumvera.+

      Udzapereka kwa iye zimene unalonjeza.+

  • Salimo 66:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ndidzalowa m’nyumba yanu ndi nsembe zopsereza zathunthu.+

      Ine ndidzakwaniritsa malonjezo anga kwa inu+

  • Salimo 116:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ndidzakwaniritsa malonjezo anga kwa Yehova,+

      Ndidzawakwaniritsa pamaso pa anthu ake onse,+

  • Mlaliki 5:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ukalonjeza kwa Mulungu usamachedwe kukwaniritsa lonjezo lako,+ chifukwa palibe amene amasangalala ndi anthu opusa.+ Uzikwaniritsa zinthu zimene walonjeza.+

  • Yona 2:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Koma ine, ndidzakutamandani ndi kupereka nsembe kwa inu.+

      Zimene ndalonjeza ndidzazikwaniritsa.+ Chipulumutso chimachokera kwa Yehova.”+

  • Nahumu 1:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 “Taonani mapazi a munthu yemwe akuyenda pamwamba pa mapiri pobweretsa uthenga wabwino.+ Iye akulengeza za mtendere. Iwe Yuda, chita zikondwerero zako.+ Kwaniritsa zimene walonjeza+ chifukwa palibe munthu aliyense wopanda pake amene adzadutsa pakati pako.+ Munthu wopanda pakeyo adzaphedwa.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena