-
Salimo 66:13Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
13 Ndidzalowa m’nyumba yanu ndi nsembe zopsereza zathunthu.+
Ine ndidzakwaniritsa malonjezo anga kwa inu+
-
Salimo 116:18Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
18 Ndidzakwaniritsa malonjezo anga kwa Yehova,+
Ndidzawakwaniritsa pamaso pa anthu ake onse,+
-
-
-