Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 12:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Kumalo amenewo, inuyo ndi mabanja anu muzidzadya zimenezi ndi kusangalala ndi zochita zanu zonse+ pamaso pa Yehova,+ chifukwa Yehova Mulungu wanu wakudalitsani.

  • Salimo 32:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Inu olungama, kondwerani chifukwa cha zimene Yehova wachita ndipo sangalalani.+

      Fuulani ndi chisangalalo inu nonse owongoka mtima.+

  • Salimo 63:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Moyo wanga wakhutira ndi gawo labwino kwambiri, wakhutira ndi zinthu zabwino kwambiri,+

      Ndipo milomo yanga ikukutamandani ndi mfuu yachisangalalo.+

  • Salimo 68:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Koma olungama asangalale,+

      Asekerere pamaso pa Mulungu,+

      Ndipo akondwere ndi kusangalala.+

  • Afilipi 4:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Nthawi zonse kondwerani mwa Ambuye.+ Ndibwerezanso, Kondwerani.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena