Deuteronomo 12:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Kumalo amenewo, inuyo ndi mabanja anu muzidzadya zimenezi ndi kusangalala ndi zochita zanu zonse+ pamaso pa Yehova,+ chifukwa Yehova Mulungu wanu wakudalitsani. Deuteronomo 32:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 Yesuruni*+ atayamba kunenepa, anayamba kupanduka.+Iwe wanenepa, wakulupala, wakhuta mopitirira muyezo.+Pamenepo iye anasiya Mulungu amene anam’panga,+Ndi kunyoza Thanthwe+ la chipulumutso chake. Nehemiya 9:35 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 35 Iwo sanakutumikireni+ ndipo sanabwerere kusiya zoipa zimene anali kuchita+ pamene anali ndi mafumu+ komanso pamene munali kuwapatsa zabwino zochuluka,+ m’dziko lalikulu ndi lachonde+ limene munawapatsa.
7 Kumalo amenewo, inuyo ndi mabanja anu muzidzadya zimenezi ndi kusangalala ndi zochita zanu zonse+ pamaso pa Yehova,+ chifukwa Yehova Mulungu wanu wakudalitsani.
15 Yesuruni*+ atayamba kunenepa, anayamba kupanduka.+Iwe wanenepa, wakulupala, wakhuta mopitirira muyezo.+Pamenepo iye anasiya Mulungu amene anam’panga,+Ndi kunyoza Thanthwe+ la chipulumutso chake.
35 Iwo sanakutumikireni+ ndipo sanabwerere kusiya zoipa zimene anali kuchita+ pamene anali ndi mafumu+ komanso pamene munali kuwapatsa zabwino zochuluka,+ m’dziko lalikulu ndi lachonde+ limene munawapatsa.