Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 20:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Mose atatero, anakweza dzanja lake n’kumenya thanthwelo kawiri ndi ndodo yake. Pamenepo madzi ambiri anayamba kutuluka, ndipo khamu lonselo linayamba kumwa madziwo limodzi ndi ziweto zawo.+

  • Salimo 78:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Iye anang’amba miyala m’chipululu+

      Kuti awapatse madzi akumwa ochuluka ngati a m’nyanja.+

  • Salimo 105:41
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 41 Anatsegula thanthwe ndipo panatuluka madzi ambiri.+

      Madziwo anayenda ngati mtsinje kudutsa m’dera lopanda madzi.+

  • Salimo 114:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Amene amasintha thanthwe kukhala dambo la madzi,+

      Ndiponso amasintha mwala wa nsangalabwi kukhala kasupe.+

  • 1 Akorinto 10:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 ndipo onse anamwa chakumwa chimodzimodzi chauzimu.+ Pakuti anali kumwa pathanthwe lauzimu+ limene linali kuwatsatira, ndipo thanthwelo+ linatanthauza Khristu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena