-
Deuteronomo 13:7Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
7 milungu ina mwa milungu ya anthu okuzungulirani, okhala pafupi nanu kapena okhala kutali, kuchokera kumalekezero ena a dziko kukafika kumalekezero ena,
-
-
Oweruza 10:6Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
6 Zitatero, ana a Isiraeli anayambanso kuchita zoipa pamaso pa Yehova,+ ndipo anayamba kutumikira Abaala,+ zifaniziro za Asitoreti,+ milungu ya ku Siriya,+ milungu ya ku Sidoni,+ milungu ya ku Mowabu,+ milungu ya ana a Amoni+ ndi milungu ya Afilisiti.+ Motero iwo anasiya Yehova ndipo sanam’tumikire.+
-