Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 19:43
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 43 Eloni, Timuna,+ Ekironi,+

  • 1 Samueli 5:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Choncho anatumiza likasa la Mulungu woona ku Ekironi.+ Ndiyeno likasa la Mulungu woona litangofika ku Ekironi, anthu a ku Ekironi anayamba kulira, kuti: “Atibweretsera likasa la Mulungu wa Isiraeli kuti atiphe ife tonse!”+

  • 1 Samueli 7:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Pamenepo, mizinda imene Afilisitiwo analanda Isiraeli inayamba kubwerera kwa Isiraeli, kuyambira ku Ekironi mpaka ku Gati, ndipo Aisiraeli analanda dera la mizindayo m’manja mwa Afilisiti.

      Choncho panakhala mtendere pakati pa Isiraeli ndi Aamori.+

  • 2 Mafumu 1:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Kenako Ahaziya ali m’nyumba yake ku Samariya, anagwa+ kuchokera pachipinda chapadenga+ kudzera pachibowo chotchinga, ndipo anavulala. Atatero anatuma amithenga kuti: “Pitani kwa Baala-zebubu+ mulungu wa ku Ekironi,+ mukafunse+ ngati ndichire matenda angawa.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena