Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 20:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Mizinda yokhayi ya anthu awa a mitundu ina imene Yehova Mulungu wanu akukupatsani monga cholowa, ndi imene simuyenera kusiyamo chilichonse chopuma chili chamoyo,+

  • Yoswa 16:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Aefuraimu analephera kupitikitsa Akanani+ amene anali kukhala ku Gezeri.+ Choncho Akananiwo akukhalabe pakati pa Aefuraimu mpaka lero,+ ndipo anayamba kuwagwiritsa ntchito yaukapolo.+

  • Oweruza 1:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Fuko la Zebuloni+ silinapitikitse anthu okhala mumzinda wa Kitironi ndi mzinda wa Nahaloli,+ moti Akananiwo anakhalabe pakati pawo+ ndipo a fuko la Zebuloni anayamba kugwiritsa ntchito yaukapolo Akananiwo.+

  • 2 Mbiri 8:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 ana onse ochokera kwa iwowa amene anatsala m’dzikomo, amene ana a Isiraeli sanawawononge,+ Solomo anali kuwagwiritsa+ ntchito yaukapolo, kufikira lero.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena