16 Mizinda yokhayi ya anthu awa a mitundu ina imene Yehova Mulungu wanu akukupatsani monga cholowa, ndi imene simuyenera kusiyamo chilichonse chopuma chili chamoyo,+
30 Fuko la Zebuloni+ silinapitikitse anthu okhala mumzinda wa Kitironi ndi mzinda wa Nahaloli,+ moti Akananiwo anakhalabe pakati pawo+ ndipo a fuko la Zebuloni anayamba kugwiritsa ntchito yaukapolo Akananiwo.+