Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 4:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Zitatero anthuwo anakhulupirira+ Mose. Atamva kuti Yehova wacheukira+ ana a Isiraeli, ndi kutinso waona nsautso yawo,+ anagwada ndi kuweramira pansi.+

  • 2 Mbiri 20:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Nthawi yomweyo Yehosafati anagwada n’kuwerama mpaka nkhope yake pansi,+ ndipo Ayuda onse ndi anthu okhala mu Yerusalemu anawerama pamaso pa Yehova kuti alambire Yehovayo.+

  • Salimo 95:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Bwerani timuweramire ndi kumupembedza.+

      Tiyeni tigwade+ pamaso pa Yehova amene ndiye Wotipanga.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena