Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 2:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Amunawo anayankha kuti: “Tikadzapanda kusunga lonjezo lathu, ifeyo tidzafe m’malo mwa inu!+ Mukasunga chinsinsi cha nkhaniyi, Yehova akadzatipatsa dziko lino, ifenso tidzakusonyezani kukoma mtima kosatha, ndipo tidzakhulupirika kwa inu.”+

  • 1 Samueli 20:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ndipo ine ndikadzakhalabe ndi moyo,+ kodi sudzandisonyeza kukoma mtima kosatha kwa Yehova kuti ndisafe?+ Kodi sudzatero?

  • 1 Samueli 30:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Pamenepo Davide anamufunsa kuti: “Kodi ungandiperekeze kumene kuli gulu la achifwambali?” Poyankha, iye anati: “Ndilumbirire+ pamaso pa Mulungu kuti sundipha, komanso kuti sundipereka m’manja mwa mbuyanga.+ Ukatero ndikuperekeza kumene kuli gulu la achifwambali.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena