Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 11:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 “Ndiyeno Yehova Mulungu wanu akadzakulowetsani m’dziko limene mukupita kukalitenga kuti likhale lanu,+ mukatchule dalitsoli paphiri la Gerizimu+ ndipo temberero mukalitchulire paphiri la Ebala.+

  • Yoswa 8:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Aisiraeli onse, atsogoleri awo,+ akapitawo awo, ndi oweruza awo anasonkhanitsidwa pamodzi. Panalinso alendo okhala pakati pawo.+ Ena anaima mbali iyi ya Likasa, ena anaima mbali inayo, pamaso pa ansembe+ achilevi. Ansembewo anali atanyamula likasa la pangano la Yehova.+ Hafu ya anthuwo inaima m’phiri la Gerizimu,+ ndipo hafu ina inaima m’phiri la Ebala,+ (monga mmene Mose mtumiki wa Yehova analamulira,)+ kuti Aisiraeliwo adalitsidwe+ choyamba.

  • Yohane 4:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Makolo athu anali kulambira m’phiri ili,+ koma anthu inu mumanena kuti Yerusalemu ndiwo malo kumene anthu ayenera kulambirirako.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena