Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 18:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Yehova ndiye thanthwe langa, malo anga achitetezo ndiponso Wopereka chipulumutso kwa ine.+

      Mulungu wanga ndiye thanthwe langa. Ine ndidzathawira kwa iye.+

      Iye ndiye chishango changa, nyanga* yanga ya chipulumutso ndiponso ndiye malo anga okwezeka achitetezo.+

  • Salimo 18:48
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 48 Iye amandipulumutsa kwa adani anga olusa.+

      Ndipo mudzandikweza pamwamba pa anthu amene amandiukira.+

      Mudzandilanditsa kwa munthu wachiwawa.+

  • Salimo 59:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Koma ine, ndidzaimba za mphamvu yanu,+

      M’mawa ndidzanena mosangalala za kukoma mtima kwanu kosatha.+

      Pakuti inu mwakhala malo anga okwezeka ndiponso achitetezo,+

      Ndiponso malo anga othawirako pa nthawi ya masautso.+

  • Salimo 124:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Moyo wathu uli ngati mbalame imene yathawa+

      Pamsampha wa munthu wogwiritsa ntchito nyambo.+

      Msamphawo wathyoka,+

      Ndipo ife tapulumuka.+

  • Mateyu 10:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Akakuzunzani mumzinda wina, muthawire mumzinda wina,+ pakuti ndithu ndikukuuzani, simudzamaliza kuzungulira+ mizinda yonse ya Isiraeli Mwana wa munthu asanafike.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena