Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 20:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Iwo ananyamuka masana pamene Beni-hadadi anali kumwa ndi kuledzera+ m’misasa, pamodzi ndi mafumu ena 32 amene anali kumuthandiza aja.

  • Miyambo 20:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Vinyo ndi wonyoza.+ Chakumwa choledzeretsa chimasokosera+ ndipo aliyense wosochera nacho alibe nzeru.+

  • Hoseya 4:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Dama, vinyo wakale ndi vinyo wotsekemera zimawononga nzeru za munthu.+

  • 1 Akorinto 6:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 akuba, aumbombo,+ zidakwa,+ olalata, kapena olanda, onsewo sadzalowa mu ufumu wa Mulungu.+

  • Aefeso 5:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ndiponso, musamaledzere naye vinyo,+ mmene muli makhalidwe oipa,+ koma khalanibe odzaza ndi mzimu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena