Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 11:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ndiyeno Nahasi Muamoni+ anapita kukamanga msasa kuti amenyane ndi mzinda wa Yabesi+ ku Giliyadi. Zitatero, amuna onse a ku Yabesi anauza Nahasi kuti: “Chita nafe pangano kuti tizikutumikira.”+

  • 2 Samueli 2:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Kenako amuna a ku Yuda+ anabwera ndi kudzoza+ Davide kumeneko kukhala mfumu ya nyumba ya Yuda.+

      Ndiyeno anthu anauza Davide kuti: “Anthu a ku Yabesi-giliyadi ndi amene anaika Sauli m’manda.”

  • 2 Samueli 21:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Chotero Davide anapita kukatenga mafupa a Sauli+ ndi mafupa a Yonatani mwana wake kwa anthu a ku Yabesi-giliyadi.+ Anthuwo ndiwo anaba mitembo ya Sauli ndi Yonatani m’bwalo la mzinda wa Beti-sani,+ kumene Afilisiti anali ataipachika,+ tsiku limene anapha Sauli paphiri la Giliboa.+

  • 1 Mbiri 10:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Anthu onse a ku Yabesi+ ku Giliyadi anamva zonse zimene Afilisiti anamuchita Sauli.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena