Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 24:45
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 45 “Ndisanamalize kulankhula+ mumtima mwanga,+ ndinangoona Rabeka akutuluka mumzindawu, atanyamula mtsuko wake paphewa. Iye anatsikira kukasupe n’kuyamba kutunga madzi.+ Pamenepo ndinamupempha kuti, ‘Chonde ndigawireko madzi ndimwe.’+

  • Nehemiya 2:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Poyankha, mfumuyo inandifunsa kuti: “Ndiye ukufuna chiyani?”+ Nthawi yomweyo ndinapemphera+ kwa Mulungu wakumwamba.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena