Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 11:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Samalani kuti mitima yanu isakopeke+ ndipo musapatuke ndi kupembedza milungu ina n’kumaiweramira.+

  • Deuteronomo 31:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Pakuti ndikudziwa bwino kuti pambuyo pa imfa yanga, mosakayikira mudzachita zinthu zokuwonongetsani+ ndipo mudzapatuka ndi kusiya njira imene ndakulamulani kuyendamo. Pamapeto pake tsoka+ lidzakugwerani, chifukwa mudzachita zoipa pamaso pa Yehova ndi kumulakwira ndi ntchito za manja anu.”+

  • Yoswa 23:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 “Tsopano khalani olimba mtima kwambiri,+ kuti musunge ndi kuchita zonse zimene zinalembedwa m’buku+ la chilamulo cha Mose, posapatukira kudzanja lamanja kapena lamanzere.+

  • 1 Samueli 12:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Koma ngati simudzamvera mawu a Yehova,+ moti n’kupandukiradi malamulo a Yehova,+ dzanja la Yehova lidzatsutsana ndi inu ndi abambo anu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena