Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 24:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Zichitike kuti, mtsikana amene ndimuuze kuti, ‘Chonde tula pansi mtsuko wako wa madzi kuti ndimweko,’ ndipo amenedi ati andiyankhe kuti, ‘Imwani, ndiponso nditungira madzi ngamila zanu kuti zimwe,’ ameneyo ndi amene mwasankhira mtumiki wanu+ Isaki. Mukachita zimenezo, ndidziwa kuti mwasonyeza mbuyanga chikondi chosatha.”+

  • Oweruza 7:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Kumeneko ukamvetsere zolankhula zawo.+ Pambuyo pake udzalimba mtima+ ndipo udzapitadi kumsasawo ndi kuuthira nkhondo.” Pamenepo, Gidiyoni ndi Pura mtumiki wake, anapita kumunsi pafupi kwambiri ndi asilikali amene anafola mwa dongosolo lomenyera nkhondo amene anali mumsasawo.

  • 1 Samueli 10:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Ndiyeno zizindikiro+ zimenezi zikachitika pa iwe, uchite chilichonse chimene ungathe,+ chifukwa Mulungu woona ali ndi iwe.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena