Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 11:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Pamenepo Uriya anayankha Davide kuti: “Likasa,+ Isiraeli ndi Yuda akukhala m’misasa, ndipo mbuyanga Yowabu pamodzi ndi atumiki anu mbuyanga+ ali mumsasa kuthengo. Ndiye ine ndikalowe m’nyumba yanga kukadya chakudya, kumwa ndi kugona ndi mkazi wanga?+ Ndithu, pali inu ndi moyo wanu,+ sindingachite zimenezo.”

  • 1 Mafumu 1:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Mfumuyo inawauza kuti: “Tengani atumiki+ a mbuye wanu, n’kukweza Solomo mwana wanga panyulu* yanga yaikazi,+ ndipo mupite naye ku Gihoni.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena